Isaiah 44:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Phindu lake nchiyani kupanga kamulungu kapena kusungunula fano lachabechabe?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndani wapanga mulungu, kapena kusungunula fano losema losapindula kanthu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndani amasema mulungu ndi kuwumba fano, limene silingamupindulire?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndani wapanga mulungu, kapena kusungunula fano losema losapindula kanthu?