Isaiah 44:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndine amene ndimauza nyanja yaikulu kuti, ‘Uma, ndipo mitsinje yakonso ndiiwumitsa.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndine amene nditi kwa nyanja yakuya, Iphwa, ndipo ndidzaumitsa nyanja zako;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndine amene ndinawuza nyanga yayikulu kuti, ‘Uma’ ndipo ndidzawumitsa mitsinje yako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndine amene nditi kwa nyanja yakuya, Iphwa, ndipo ndidzaumitsa nyanja zako;