Isaiah 44:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndine amene ndimanena za Kirusi kuti ‘Iye uja ndi mbusa wanga, adzachita zonse zimene ndikulinga! Adzalamula kuti Yerusalemu amangidwenso, ndipo kuti maziko a Nyumba ya Mulungu aikidwe.’ ”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kunena za Kirusi, Iye ndiye mbusa wanga, ndipo adzachita zofuna zanga zonse; ndi kunena za Yerusalemu, Adzamangidwa; ndi kwa Kachisi, Maziko ako adzaikidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndine amene ndinanena kwa Koresi kuti, ‘Iye ndiye mʼbusa wanga,’ ndipo adzachita zonse zimene ndikufuna; iye adzalamula kuti, ‘Yerusalemu amangidwenso’ ndi kuti, ‘Maziko a Nyumba ya Mulungu ayikidwenso.’ ”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi kunena za Koresi, Iye ndiye mbusa wanga, ndipo adzacita zofuna zanga zonse; ndi kunena za Yerusalemu, Adzamangidwa; ndi kwa Kacisi, Maziko ako adzaikidwa.