Isaiah 45:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta, Woyera uja wa Israele ndiponso Mlengi wake, akunena kuti, “Kodi iwe ungandifunse za ana anga, kapena kundilamula pa zokhudza ntchito zanga?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atero Yehova Woyera wa Israele ndi Mlengi wake, Ndifunse Ine za zinthu zimene zilinkudza; za ana anga amuna, ndi za ntchito ya manja anga, ndilamulireni Ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Yehova Woyerayo wa Israeli, ndiponso Mlengi wake akunena, zokhudza zinthu zimene zikubwera ndi izi: Kodi iwe ukundifunsa za ana anga, kapena kundilamula pa zokhudza ntchito zanga?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atero Yehova Woyera wa Israyeli ndi Mlengi wace, Ndifunse Ine za zinthu zimene zirinkudza; za ana anga amuna, ndi za nchito ya manja anga, ndilamulireni Ine.