Isaiah 45:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Pokamba za Ine adzanena kuti, ‘Chilungamo ndiponso mphamvu zimapezeka mwa Chauta yekha. Onse amene ankamugalukira adzabwera kwa Iye ndipo adzachita manyazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mwa Yehova yekha, wina adzati kwa Ine, muli chilungamo ndi mphamvu; ngakhale kwa Iyeyo anthu adzafika, ndi onse amene anamkwiyira, adzakhala ndi manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo adzanene kwa Ine kuti, ‘Chilungamo ndi mphamvu zimapezeka mwa Yehova yekha.’ ” Onse amene anamuwukira Iye adzabwera kwa Iye ndipo adzachita manyazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mwa Yehova yekha, wina adzati kwa Ine, muli cilungamo ndi mphamvu; ngakhale kwa Iyeyo anthu adzafika, ndi onse amene anamkwiyira, adzakhala ndi manyazi.