Isaiah 46:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyamazo zikuŵerama ndi kufuna kugwa naye katunduyo, sizikutha kumpulumutsa. Izo zomwe zikupita ku ukapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Milunguyo iwerama, igwada pansi pamodzi; singapulumutse katundu, koma iyo yeni yalowa m'ndende.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyamazo zikuwerama ndi kufuna kugwa ndi milunguyo; sizikutha kupulumutsa katunduyo, izo zomwe zikupita ku ukapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Milunguyo iwerama, igwada pansi pamodzi; singapulumutse katundu, koma iyo yeni yalowa m'ndende.