Isaiah 48:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidakuyeretsa, komatu osati ngati siliva, ndidakuyesa m'ng'anjo yamasautso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taona ndakuyenga, koma si monga siliva, ndakuyesa iwe m'ng'anjo ya masautso.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani, ndinakuyeretsani ngati siliva; ndinakuyesani mʼngʼanjo yamasautso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taona ndakuyenga, koma si monga siliva, ndakuyesa iwe m'ng'anjo ya masautso.