Isaiah 48:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kuti anthu alemekeze dzina langa ndikuchedwetsa mkwiyo wanga. Kuti anthu aone ulemerero wanga ndikukulezera ukali wanga, kuti ndisakuwononge kotheratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa cha dzina langa ndidzachedwetsa mkwiyo wanga, ndi chifukwa cha kutamanda kwanga ndidzakulekerera, kuti ndisakuchotse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndikuchedwetsa mkwiyo wanga chifukwa cha dzina langa. Ndikukulezerani ukali wanga kuti anthu andilemekeze. Sindidzakuwonongani kotheratu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa ca dzina langa ndidzacedwetsa mkwiyo wanga, ndi cifukwa ca kutamanda kwanga ndidzakulekerera, kuti ndisakucotse.