Isaiah 49:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma anthu a ku Ziyoni adati, “Chauta watisiya ife, Ambuye atiiŵala.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Ziyoni anati, Yehova wandisiya ine, ndipo Ambuye wandiiwala ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Ziyoni anati, “Yehova wandisiya, Ambuye wandiyiwala.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Ziyoni anati, Yehova wandisiya ine, ndipo Ambuye wandiiwala ine.