Isaiah 51:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Palibe wina wokutsogolera mwa ana amene udaŵabala. Palibe ndi mmodzi yemwe wokugwira pa dzanja mwa ana amene udaŵalera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Palibenso wina wakumtsogolera mwa ana amuna onse, amene iye anawabala; palibe wina amgwira dzanja mwa ana onse anawalera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwa ana onse amene anabereka, panalibe ndi mmodzi yemwe anamutsogolera; mwa ana onse amene analera, panalibe ndi mmodzi yemwe anamugwira dzanja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Palibenso wina wakumtsogolera mwa ana amuna onse, amene iye anawabala; palibe wina amgwira dzanja mwa ana onse anawalera.