Isaiah 52:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akuti, “Mtumiki wanga adzapambana pa ntchito yake. Adzakwezedwa ndi kulemekezedwa, ndipo adzalandira ulemu waukulu kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, Mtumiki wanga adzachita mwanzeru; adzakwezedwa ndi kutukulidwa pamwamba, nadzakhala pamwambamwamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani, mtumiki wanga adzapambana pa ntchito yake adzakwezedwa ndi kulemekezedwa ndipo adzalandira ulemu waukulu kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, Mtumiki wanga adzacita mwanzeru; adzakwezedwa ndi kutukulidwa pamwamba, nadzakhala pamwambamwamba.