Isaiah 55:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Mudziŵe kuti iye uja ndidamsankha kuti akhale mboni yanga kwa mitundu ya anthu, kuti akhale mtsogoleri ndi wolamulira anthu ambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, ndampereka iye akhale mboni ya anthu, wotsogolera ndi wolamulira anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani, ine ndamusankha kuti akhale mboni yanga kwa mitundu ya anthu, kuti akhale mtsogoleri ndi wolamulira mitundu ya anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, ndampereka iye akhale mboni ya anthu, wotsogolera ndi wolamulira anthu.