Isaiah 57:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Palibe mtendere kwa oipa,” akutero Mulungu wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Palibe mtendere, ati Mulungu wanga, kwa oipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Palibe mtendere kwa oyipa,” akutero Mulungu wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Palibe mtendere, ati Mulungu wanga, kwa oipa.