Isaiah 59:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akuuza anthu ake kuti, “Ndidzabwera ku Yerusalemu kudzapulumutsa a fuko la Yakobe amene adaleka machimo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Mombolo adzafika ku Ziyoni, ndi kwa iwo amene atembenuka kusiya kulakwa mwa Yakobo, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Mpulumutsi adzabwera ku Ziyoni kudzapulumutsa anthu a fuko la Yakobo amene analapa machimo awo,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Mombolo adzafika ku Ziyoni, ndi kwa iwo amene atembenuka kusiya kulakwa mwa Yakobo, ati Yehova.