Isaiah 61:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adzamanganso mabwinja akale a mzinda, adzautsa nyumba zimene zidaaonongeka. Adzakonzanso mizinda imene idaapasuka, ndiponso malo osiyidwa chiyambire cha kalekale.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo adzamanga mabwinja akale, nadzamanga pa miunda yakale, nadzakonzanso midzi yopasuka, mabwinja a mibadwo yambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Adzamanganso mabwinja akale a mzinda ndipo malo amene anawonongeka kalekale aja adzakonzanso. Adzakonzanso mizinda imene inapasuka, imene yakhala yowonongeka kwa nthawi yayitali kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo adzamanga mabwinja akale, nadzamanga pa miunda yakale, nadzakonzanso midzi yopasuka, mabwinja a mibadwo yambiri.