Isaiah 61:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana ao adzakhala odziŵika pakati pa anthu a mitundu ina, zidzukulu zaonso zidzakhala zotchuka pakati pa anthu onse. Aliyense woŵaona adzazindikira kuti ndi anthu amene Ine Chauta ndidaŵadalitsa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ana ao adzadziwidwa mwa amitundu, ndi obadwa ao mwa anthu; onse amene awaona adzawazindikira kuti iwo ndiwo ana amene Yehova wadalitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana awo adzakhala odziwika pakati pa mitundu ya anthu ndipo adzukulu awo adzakhala otchuka pakati pa anthu a mitundu ina. Aliyense wowaona adzazindikira kuti ndi anthu amene Yehova wawadalitsa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ana ao adzadziwidwa mwa amitundu, ndi obadwa ao mwa anthu; onse amene awaona adzawazindikira kuti iwo ndiwo ana amene Yehova wadalitsa.