Isaiah 63:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mzimu wa Chauta udaŵapumitsa, monga m'mene ng'ombe zimapumulira ku dambo.” Motero Inu Chauta mudatsogolera anthu anu, kuti dzina lanu lilemekezeke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga ng'ombe zotsikira kuchigwa mzimu wa Yehova unawapumitsa; chomwecho inu munatsogolera anthu anu kudzitengera mbiri yaulemerero.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mzimu Woyera unawapumulitsa ngati mmene ngʼombe zimapumulira. Umu ndi mmene Inu munatsogolera anthu anu kuti dzina lanu lilemekezeke.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga ng'ombe zotsikira kucigwa mzimu wa Yehova unawapumitsa; comweco inu munatsogolera anthu anu kudzitengera mbiri yaulemerero.