Isaiah 64:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta, bwanji osang'amba mlengalenga kuti mutsike pansi? Bwanji osati mapiri agwedezeke poona Inu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwenzi mutang'amba kumwamba ndi kutsikira pansi, kuti mapiri agwedezeke pamaso panu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu Yehova, bwanji mukanangongʼamba mlengalenga ndi kutsika pansi, kuti mapiri agwedezeke pamaso panu!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwenzi mutang'amba kumwamba ndi kutsikira pansi, kuti mapiri agwedezeke pamaso panu;