Isaiah 65:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo adzaimba mokondwa, koma inu mudzalira kwambiri chifukwa chovutika mu mtima. Mudzalira mofuula chifukwa cha kumva kuŵaŵa mu mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
taonani, atumiki anga adzaimba ndi mtima wosangalala, koma inu mudzalira ndi mtima wachisoni; ndipo mudzafuula chifukwa cha kusweka mzimu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atumiki anga adzayimba mosangalala, koma inu mudzalira kwambiri chifukwa chovutika mu mtima ndipo mudzalira mofuwula chifukwa mudzamva kuwawa mu mtima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
taonani, atumiki anga adzayimba ndi mtima wosangalala, koma inu mudzalira ndi mtima wacisoni; ndipo mudzapfuula cifukwa ca kusweka mzimu.