Isaiah 65:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sadzagwira ntchito pachabe, kapena kubereka ana kuti aone tsoka, chifukwa adzakhala anthu odalitsidwa ndi Chauta, iwowo ndi zidzukulu zao zomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwo sadzagwira ntchito mwachabe, pena kubalira tsoka; pakuti iwo ndiwo mbeu ya odalitsidwa a Yehova, ndi obadwa ao adzakhala pamodzi ndi iwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sadzagwira ntchito pachabe kapena kubereka ana kuti aone tsoka; chifukwa adzakhala anthu odalitsidwa ndi Yehova, iwowo pamodzi ndi adzukulu awo omwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwo sadzagwira nchito mwacabe, pena kubalira tsoka; pakuti iwo ndiwo mbeu ya odalitsidwa a Yehova, ndi obadwa ao adzakhala pamodzi ndi iwo.