Isaiah 65:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amakatandala ku manda, amachezera kumalo obisika usiku. Amadya nyama yankhumba, namamwa msuzi wa nyama zoperekera nsembe zachikunja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene akhala pakati pa manda, ndi kugona m'malo am'tseri; amene adya nyama ya nkhumba, ndi msuzi wa zinthu zonyansa uli m'mbale zao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amakatandala ku manda ndipo amakachezera usiku wonse kumalo obisika. Amadya nyama ya nkhumba, ndipo mʼmiphika mwawo muli msunzi wa nyama yodetsedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amene akhala pakati pa manda, ndi kugona m'malo am'tseri; amene adya nyama ya nkhumba, ndi msuzi wa zinthu zonyansa uli m'mbale zao;