Isaiah 65:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndatsimikiza kale za chilango chao, ndipo mlandu wao ndaulemba kale. Ndidzaŵalanga chifukwa cha machimo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, chalembedwa pamaso panga; sindidzakhala chete, koma ndidzabwezera, inde ndidzabwezera pa chifuwa chao,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo; sindidzakhala chete koma ndidzawalanga kwathunthu chifukwa cha machimo awo
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, calembedwa pamaso panga; sindidzakhala cete, koma ndidzabwezera, inde ndidzabwezera pa cifuwa cao,