Isaiah 7:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adalankhulanso ndi Ahazi kudzera mwa mneneri Yesaya kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova ananenanso kwa Ahazi nati,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anayankhulanso ndi Ahazi,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova ananenanso kwa Ahazi nati,