Isaiah 7:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Azidzadya chambiko ndi uchi, mpaka atadziŵa kukana choipa ndi kusankha chabwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye adzadya mafuta ndi uchi, pamene adziwa kukana choipa ndi kusankha chabwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Azidzadya chambiko ndi uchi, mpaka atadziwa kukana choyipa ndi kusankha chabwino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye adzadya mafuta ndi uci, pamene adziwa kukana coipa ndi kusankha cabwino.