Isaiah 7:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsiku limenelo mwina munthu adzangosunga ng'ombe yaing'ono yamkaka ndi mbuzi ziŵiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo padzakhala tsiku limenelo, kuti munthu adzaweta ng'ombe yaikazi yaing'ono, ndi nkhosa ziwiri;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsiku limenelo adzangosunga ngʼombe yayikazi yayingʼono ndi mbuzi ziwiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo padzakhala tsiku limenelo, kuti munthu adzaweta ng'ombe yaikazi yaing'ono, ndi nkhosa ziwiri;