Isaiah 7:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu adzafika kumeneko kudzachita uzimba ali ndi uta ndi mivi, popeza kuti m'dziko monsemo mudzakhala mkandankhuku ndi minga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu adzafikako ndi mivi ndi uta; pakuti dziko lonse lidzakhala la lunguzi ndi minga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu adzapita kumeneko kukachita uzimba ali ndi uta ndi mivi, popeza kuti mʼdziko monsemo mudzakhala mkandankhuku ndi minga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu adzafikako ndi mibvi ndi uta; pakuti dziko lonse lidzakhala la lunguzi ndi minga.