Isaiah 7:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo m'mapiri monse m'mene kale munkalimidwa, anthu sadzafikako, kuwopa mkandankhukuwo ndi mingayo. Malowo adzasanduka odyetserako ng'ombe ndi nkhosa basi.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo zitunda zonse zinalimidwa ndi khasu, iwe sudzafikako chifukwa cha kuopa lunguzi ndi minga, koma pomwepo padzakhala potumizira ng'ombe ndi popondaponda nkhosa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo mʼmapiri monse mʼmene kale munkalimidwa ndi khasu, simudzapitamo kuopa mkandankhuku ndi minga; malowo adzasanduka odyetserako ngʼombe ndi nkhosa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo zitunda zonse zinalimidwa ndi khasu, iwe sudzafikako cifukwa ca kuopa lunguzi ndi minga, koma pomwepo padzakhala potumizira ng'ombe ndi popondaponda nkhosa.