Isaiah 7:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mfumu ya ku Siriya ndi mfumu ya ku Efuremu apangana kuti akuchiteni choipa. Akunena kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa Aramu ndi Efuremu, ndi mwana wa Remaliya anapangana kukuchitira zoipa, nati,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mfumu ya Siriya, Efereimu ndi mwana wa Remaliya apangana kuti akuchitire choyipa. Akunena kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa Aramu ndi Efraimu, ndi mwana wa Remaliya anapangana kukucitira zoipa, nati,