Isaiah 7:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
‘Tiyeni tikalimbane ndi dziko la Yuda, tikaliwopse. Tikaligonjetse kuti likhale lathu, ndipo tikalonge ufumu mwana wa Tabeele kumeneko.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tiyeni, tikwere, timenyane ndi Yuda, timvute; tiyeni, tidzigumulire mpata, pamenepo tikhazike mfumu pakati pake, ngakhale mwana wamwamuna wa Tabeele;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
‘Tiyeni tikalimbane ndi Yuda. Tiyeni tiliwononge ndi kuligawa; tiligawane pakati pathu, ndipo tilonge ufumu mwana wa Tabeeli kumeneko.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tiyeni, tikwere, timenyane ndi Yuda, timbvute; tiyeni, tidzigumulire mpata, pamenepo tikhazike mfumu pakati pace, ngakhale mwana wamwamuna wa Tabeeli;