Isaiah 7:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dziko la Efuremu limagonera pa likulu lake Samariya, ndipo Samariya amagonera pa mfumu yake Peka. Mukapanda kulimbika pa chikhulupiriro chanu, ndithu simudzalimba konse.’ ”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo mutu wa Efuremu ndi Samariya, ndi mutu wa Samariya ndi mwana wa Remaliya, mukapanda kukhulupirira ndithu simudzakhazikika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Dziko la Efereimu limadalira Samariya ndipo Samariya amadalira mwana wa Remaliya basi. Mukapanda kulimbika pa chikhulupiriro chanu, ndithu simudzalimba konse.’ ”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo mutu wa Efraimu ndi Samariya, ndi mutu wa Samariya ndi mwana wa Remaliya, mukapanda kukhulupirira ndithu simudzakhazikika.