Isaiah 9:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngakhale njerwa zagumuka, ife tidzamanga ndi miyala yosema. Ngakhale mitanda yamkuyu yagwetsedwa, ife tidzaika mitanda yamkungudza m'malo mwake.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njerwa zagwa, koma ife tidzamanga ndi miyala yosema; mikuyu yagwetsedwa, koma tidzaisinthanitsa ndi mikungudza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngakhale njerwa zagumuka, koma ife tidzamanga ndi miyala yosema. Mitanda ya mkuyu yagwetsedwa, koma ife tidzayika mitanda ya mkungudza mʼmalo mwake.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njerwa zagwa, koma ife tidzamanga ndi miyala yosema; mikuyu yagwetsedwa, koma tidzaisinthanitsa ndi mikungudza.