Isaiah 9:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo sadabwerere kwa Mulungu amene adaŵakantha uja, sadalape ndi kufunafuna Chauta Wamphamvuzonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anthu sanatembenukire kwa Iye amene anawamenya, ngakhale kufuna Yehova wa makamu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma anthu sanabwerere kwa amene anawakantha uja, ngakhale kufunafuna Yehova Wamphamvuzonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anthu sanatembenukire kwa Iye amene anawamenya, ngakhale kufuna Yehova wa makamu.