James 1:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo mbale wolemera nayenso anyadire pamene Mulungu amtsitsa, pakuti adzatha ngati duŵa la udzu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti adzapita monga duwa la udzu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma olemera anyadire pamene atsitsidwa, chifukwa adzatha ngati duwa lakuthengo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti adzapita monga duwa la udzu,