James 3:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Abale anga, musachuluke ofuna kukhala aphunzitsi, chifukwa monga mudziŵa, aphunzitsife tidzaweruzidwa mouma koposa anthu ena onse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Abale anga, ambiri musakhale aphunzitsi chifukwa mumadziwa kuti aphunzitsife tidzaweruzidwa mowuma kuposa anthu ena onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa.