James 5:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Abale anga, wina mwa inu akasokera pa kusiya choona, mnzake nkumubweza,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Abale anga, ngati wina wa inu asochera posiyana ndi choonadi, ndipo ambweza iye mnzake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Abale anga, ngati mmodzi wa inu apatuka pa choonadi ndipo wina wake ndi kumubweza,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Abale anga, ngati wina wa inu asocera posiyana ndi coonadi, ndipo ambweza iye mnzace;