James 5:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inunso khazikani mtima. Limbani mtima, pakuti Ambuye ali pafupi kubwera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Lezani mtima inunso, limbitsani mitima yanu; pakuti kudza kwake kwa Ambuye kuyandikira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inunso mukhale owugwira mtima ndi osasinthika chifukwa Ambuye ali pafupi kubwera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Lezani mtima inunso, limbitsani mitima yanu; pakuti kudza kwace kwa Ambuye kuyandikira.