Jeremiah 1:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adalankhula naye pa nthaŵi ya Yosiya, mfumu ya ku Yuda, mwana wa Amoni, pa chaka cha khumi ndi chitatu cha ufumu wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene anamdzera mau a Yehova masiku a Yosiya mwana wake wa Amoni, mfumu ya Ayuda chaka chakhumi ndi chitatu cha ufumu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawuwa Yehova anayankhula naye mʼchaka cha 13 cha ulamuliro wa Yosiya mwana wa Amoni mfumu ya Yuda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amene anamdzera mau a Yehova masiku a Yosiya mwana wace wa Amoni, mfumu ya Ayuda caka cakhumi ndi citatu ca ufumu wace.