Jeremiah 1:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usaŵaope, Ine ndili nawe, ndidzakupulumutsa,” akuterotu Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usaope nkhope zao; chifukwa Ine ndili ndi iwe kuti ndikulanditse iwe, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usawaope, pakuti Ine ndili nawe, ndipo ndidzakupulumutsa,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usaope nkhope zao; cifukwa Ine ndiri ndi iwe kuti ndikulanditse iwe, ati Yehova.