Jeremiah 10:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mafanowo ngachabechabe, ayenera kuŵaseka, ndipo pamene anthuwo adzalangidwe, mafanowo adzaonongeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndiwo chabe, ndiwo chiphamaso; pa nthawi ya kulangidwa kwao adzatha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mafanowo ndi achabechabe, zinthu zosekedwa nazo. Pamene anthuwo azidzaweruzidwa, mafanowo adzawonongedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiwo cabe, ndiwo ciphamaso; pa nthawi ya kulangidwa kwao adzatha.