Jeremiah 10:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Langizeni, Inu Chauta, koma mwachilungamo. Musandikwiyire kuti mungandiwononge.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova, mundilangize, koma ndi chiweruzo; si m'mkwiyo wanu, mungandithe psiti.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu Yehova, langizeni, komatu mwachilungamo, osati ndi mkwiyo wanu, mungandiwononge kotheratu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova, mundilangize, koma ndi ciweruzo; si m'mkwiyo wanu, mungandithe psiti.