Jeremiah 12:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komatu ngati mtundu wina uliwonse sudzamvera Ine, ndidzauwononga kotheratu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ngati sakumva, ndidzazula mtundu umene wa anthu, kuuzula ndi kuuononga, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati mtundu wina uliwonse sudzamvera, Ine ndidzawuchotsa ndi kuwuwonongeratu,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ngati sakumva, ndidzazula mtundu umene wa anthu, kuuzula ndi kuuononga, ati Yehova.