Jeremiah 13:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zokuyenerani nzimenezi, chilango chimene ndakukonzerani chifukwa choti mwandiiŵala, mwakhala mukudalira milungu yonama,” akuterotu Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ichi ndi chogwera chako, gawo la muyeso wako wa kwa Ine, ati Yehova; chifukwa wandiiwala Ine, ndi kukhulupirira zonama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Limeneli ndiye gawo lanu, chilango chimene ndakukonzerani chifukwa chondiyiwala Ine ndi kutumikira milungu yabodza, akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ici ndi cagwera cako, gawo la muyeso wako wa kwa Ine, ati Yehova; cifukwa wandiiwala Ine, ndi kukhulupirira zonama.