Jeremiah 14:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake Chauta adandiwuza kuti, “Usaŵapempherere anthu ameneŵa, kuŵafunira zabwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova anati kwa ine, Usapempherere anthu awa zabwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Usawapempherere anthu awa kuti zinthu ziwayendere bwino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anati kwa ine, Usapempherere anthu awa zabwino.