Jeremiah 14:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ukaŵauze kuti, ‘Maso anga adze misozi kosalekeza usiku ndi usana. Pakuti anthu anga osankhidwa ali ndi bala lalikulu, akanthidwa kwamphamvu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo udzati kwa iwo mau awa, Maso anga agwe misozi usana ndi usiku, asaleke; pakuti namwali mwana wa anthu anga wasweka ndi kusweka kwakukulu, ndi bala lopweteka kwambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Awuze mawu awa: “ ‘Maso anga akugwetsa misozi kosalekeza usana ndi usiku; chifukwa anthu anga okondedwa apwetekeka kwambiri, akanthidwa kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo udzati kwa iwo mau awa, Maso anga agwe misozi usana ndi usiku, asaleke; pakuti namwali mwana wa anthu anga wasweka ndi kusweka kwakukuru, ndi bala lopweteka kwambiri.