Jeremiah 14:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Yuda akulira, mizinda yake ikuvutika, anthu ake adzigwetsa pansi mwachisoni. Kulira kwa anthu a mu Yerusalemu kwakula.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yuda alira, ndipo zipata zake zilefuka, zikhala pansi zovekedwa ndi zakuda; mfuu wa Yerusalemu wakwera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Yuda akulira, mizinda yake ikuvutika; anthu ake adzigwetsa pansi mwachisoni, kulira kwa Yerusalemu kwakula.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yuda alira, ndipo zipata zace zilefuka, zikhala pansi zobvekedwa ndi zakuda; mpfuu wa Yerusalemu wakwera.