Jeremiah 14:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pansi mpouma kotheratu, poti kulibe mvula. Alimi akuchita manyazi, ndipo adziphimba kumaso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa cha nthaka yochita ming'alu, pakuti panalibe mvula padziko, olima ali ndi manyazi, afunda mitu yao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza pansi pawumiratu chifukwa kulibe madzi, alimi ali ndi manyazi ndipo amphimba nkhope zawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa ca nthaka yocita ming'aru, pakuti panalibe mvula padziko, olima ali ndi manyazi, apfunda mitu yao.