Jeremiah 14:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mbaŵala yomwe ikusiya mwana wake wakhanda ku thengo chifukwa choti kulibe msipu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inde, mbawalanso ya m'thengo ibala nisiya ana ake, chifukwa mulibe udzu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale mbawala yayikazi ikusiya mwana wake wakhanda ku thengo chifukwa kulibe msipu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inde, nswalanso ya m'thengo ibala nisiya ana ace, cifukwa mulibe maudzu.