Jeremiah 16:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono iwe udzayankhe kuti, ‘Nchifukwa chakuti makolo anu adandisiya Ine,’ akuterotu Chauta. ‘Adatsata milungu ina, namaitumikira ndi kumaipembedza. Adandisiya Ine, ndipo sadamvere malamulo anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo uziti kwa iwo, Chifukwa makolo anu anandisiya Ine, ati Yehova, natsata milungu ina, naitumikira, naigwadira, nandisiya Ine, osasunga chilamulo changa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo ukawawuze kuti, ‘Nʼchifukwa chakuti makolo anu anandisiya Ine,’ akutero Yehova, ‘ndi kutsatira milungu ina, kuyitumikira ndi kuyipembedza. Iwo anandisiya Ine ndipo sanasunge lamulo langa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo uziti kwa iwo, Cifukwa makolo anu anandisiya Ine, ati Yehova, natsata milungu yina, naitumikira, naigwadira, nandisiya Ine, osasunga cilamulo canga;