Jeremiah 16:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Usadzakwatire, usadzabale ana aamuna kapena aakazi ku malo ano.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usatenge mkazi, usakhale ndi ana aamuna ndi aakazi m'malo muno.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Usadzakwatire ndi kubereka ana aamuna kapena aakazi malo ano
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usatenge mkazi, usakhale ndi ana amuna ndi akazi m'malo muno.