Jeremiah 16:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Usadzaloŵe m'nyumba m'mene muli phwando, kuti udye nao ndi kumwa nao,”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndipo usalowe mʼnyumba mmene muli madyerero, nʼkukhala pansi ndi kudya ndi kumwa nawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa.